Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 11/07 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2007
  • Nkhani Yofanana
  • Kukhulupirira Ena N’kofunika Kwambiri Kuti Munthu Akhale Wosangalala
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Muzikhulupirira Abale Anu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi Muyenera Kukhulupirira Baibulo?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Kodi Muyenera Kukhulupirira Baibulo?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Yambani Kuphunzira Baibulo
Onani Zambiri
Galamukani!—2007
g 11/07 tsamba 1-2

Zamkatimu

October 2007

Magazini Yapadera

Kodi Tiyenera Kukhulupirira Baibulo?

Palibe buku lina lililonse limene lafalitsidwa kwambiri kuposa Baibulo. Koma kodi tingadziwe bwanji kuti uthenga wa m’Baibulo ndi wochokera kwa Mulungu? Onani m’magaziniyi umboni, monga woperekedwa ndi mbiri yakale ndiponso sayansi, womwe ungakuthandizeni kuyankha funsoli.

3 Tilikhulupirire Kapena Ayi?

4 Buku Lapadera

5 Chifukwa Chake Tiyenera Kukhulupirira Baibulo

1. Ndi Lolondola Pankhani za Mbiri Yakale

2. Olemba Ake Ananena Zoona Zokhazokha

3. Nkhani Zake N’zogwirizana

4. Ndi Lolondola Pankhani za Sayansi

5. Kukwaniritsidwa kwa Ulosi

10 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Mlembi wa Baibulo Ndani?

Ngati Baibulo linalembedwa ndi anthu, kodi lingakhale bwanji Mawu a Mulungu?

12 Baibulo Lakumana ndi Zambiri

Onani mavuto amene Baibulo ladutsa, mpaka kukhala buku lotchuka kwambiri padziko lonse.

15 Zinthu Zakale Zimasonyeza Kuti Baibulo Ndi Lolondola

Werengani za zinthu zakale zochititsa chidwi zimene zimapereka umboni woti Baibulo ndi lolondola.

19 Kodi Baibulo Limanena za Chiyani?

M’Baibulo muli mfundo yaikulu imodzi. Kodi mukuidziwa?

22 Zoona Kapena Zopeka?

Werengani za zikhulupiriro zopeka zisanu zokhudza Baibulo zimene anthu ambiri ali nazo.

23 Kodi Muyenera Kukhulupirira Malangizo a M’Baibulo?

Onani mmene Baibulo lingakuthandizireni kukhala ndi moyo wabwino ndi wosangalala.

26 Zimene Achinyamata Amadzifunsa . . .

Ndizitsatira Mfundo za M’Baibulo Chifukwa Chiyani?

Onani chimene chimachititsa achinyamata ambiri kuona kuti malangizo a m’Baibulo ndi ofunika kwambiri.

29 Baibulo Ndi Umboni Wosatha wa Chikondi cha Mulungu

Sikuti Baibulo langokhala buku labwino. Onani chifukwa chake.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

© The Trustees of the Chester Beatty Library, Dublin

Musée du Louvre, Paris

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena