Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 11/08 tsamba 22-31
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
  • Galamukani!—2008
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Chithunzichi Chalakwika Pati?
  • Kuchokera M’magazini Ino
  • Zithunzi Zoti Ana Apeze
  • Ndani Ali M’gulu la Makolo a Yesu?
  • MAYANKHO A MAFUNSO A PA TSAMBA 31
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2008
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2008
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2008
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2008
Onani Zambiri
Galamukani!—2008
g 11/08 tsamba 22-31

Kodi Mungayankhe Bwanji?

Kodi Chithunzichi Chalakwika Pati?

Tchulani zinthu zitatu pa chithunzichi zomwe sizikugwirizana ndi nkhani ya m’Baibulo ya pa Genesis 7:1-9, 13-16, 23; 8:15-19.

1. ․․․․․

2. ․․․․․

ZOKUTHANDIZANI: Yerekezerani Levitiko 11:3 ndi Deuteronomo 14:4.

3. ․․․․․

ZOKUTHANDIZANI: Yerekezerani ndi Deuteronomo 14:7-19.

KAMBIRANANI:

Kodi Nowa anathandizidwa bwanji ndi ana ake komanso azipongozi ake? Kodi mungatsanzire bwanji ana a Nowa?

Kuchokera M’magazini Ino

Yankhani mafunsowa, ndipo lembani vesi kapena mavesi a m’Baibulo omwe akusowapo.

TSAMBA 6 Kodi munthu wokonda ndalama sangakhale ndi chiyani? Mlaliki 5:․․․

TSAMBA 9 Kodi ndi anthu otani amene angakhale osangalala? Mateyo 5:․․․

TSAMBA 18 Kodi munthu sayenera kuchita chiyani popemphera? Mateyo 6:․․․

TSAMBA 28 Kodi tizitani tikakhala ndi nkhawa? 1 Petulo 5:․․․

Zithunzi Zoti Ana Apeze

Kodi mungapeze zithunzi izi m’magazini ino? Fotokozani zimene zikuchitika pa chithunzi chilichonse.

Ndani Ali M’gulu la Makolo a Yesu?

Onani zokuthandizani kupeza yankho. Onaninso malembawo. Kenako lembani mayina olondola pa mizereyi.

4. ․․․․․

ZOKUTHANDIZANI: Ngakhale kuti bambo anga anali ndi khalidwe loipa, ine ndinali mfumu imene ‘inaumirira Yehova.’

Werengani 2 Mafumu 18:1-6.

5. ․․․․․

ZOKUTHANDIZANI: Ndinagwiritsa ntchito molakwika mphamvu zanga mwa kupha anthu ambiri osachimwa.

Werengani 2 Mafumu 21:16.

6. ․․․․․

ZOKUTHANDIZANI: Ndinatengera khalidwe loipa la bambo anga ndipo ndinaphedwa ndi anyamata anga.

Werengani 2 Mafumu 21:19-23.

◼ Mayankho ali pa tsamba  22

MAYANKHO A MAFUNSO A PA TSAMBA 31

1.  Chingalawa sichinali chosongoka kumbuyo ndi kutsogolo.

2. Nowa analowetsa m’chingalawa nyama 7 “zoyera,” monga nkhosa.

3 Nowa analowetsa m’chingalawa nyama ziwiri zokha pamtundu uliwonse wa nyama ‘zodetsedwa.’

4 Hezekiya.—Mateyo 1:9.

5. Manase.—Mateyo 1:10.

6. Amoni.—Mateyo 1:10.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena