Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 7/10 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2010
  • Nkhani Yofanana
  • Muziona Kuti Abale ndi Alongo Anu Osamva Ndi Ofunika Kwambiri
    Nsanja ya Olonda—2009
  • “Kuphunzira Baibulo Kukuthandiza Anthu Osamva”
    Galamukani!—2010
  • Kumvetsera ndi Maso Anu
    Galamukani!—1998
  • ‘Yehova Wawalitsa Nkhope Yake pa Iwo’
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Galamukani!—2010
g 7/10 tsamba 1-2

Zamkatimu

July 2010

Ngati Ntchito Yatha Kodi Mungasamale Bwanji Ndalama?

Ngati ntchito yakutherani, kodi mungatani kuti muzikwanitsa kukhala moyo wosalira zambiri?

3 “Pepani, Ntchito Yanu Yatha”

4 “Musade Nkhawa za Tsiku Lotsatira”

6 Kodi Mungasamale Bwanji Ndalama Zochepa Zimene Mumapeza?

14 Khoti Lina ku Spain Linagamula Kuti Mayi Wina Ali ndi Ufulu Wolera Ana Ake

15 Anyani Ochititsa Chidwi a ku Indonesia

19 Kukwera Phiri Lalitali N’koopsa Kodi Mungatani Mutadwala Pokwera Phiri?

21 Dzina la Mulungu Likulengezedwabe

22 Zochitika Padzikoli

23 “Mbalame Zazikulu Zouluka Mogometsa”

28 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Akazi Ayenera Kukhala Atumiki Mumpingo?

30 Panagona Luso!

Diso la Kadziwotche

31 Zoti Banja Likambirane

32 ‘Buku Lothandiza Kwambiri’

Kodi Ndingakwanitse Kukakhala Pandekha? 10

Nkhaniyi ikuthandizani kudziwa ngati mwakonzeka kuchoka pakhomo pa makolo anu.

“Kuphunzira Baibulo Kukuthandiza Anthu Osamva” 26

Munthu wina wolemba nkhani wa ku Czech Republic anayamikira Mboni za Yehova chifukwa chothandiza anthu osamva. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chimene chinamupangitsa kunena zimenezi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena