Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g17 No. 4 tsamba 2
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Galamukani!—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mungatani Kuti Muzigwiritsa Ntchito Bwino Nthawi?
    Galamukani!—2014
  • Kodi Inuyo Mumatanganidwa Kwambiri?
    Galamukani!—2017
  • Pakachitika Ngozi Zogwa Mwadzidzidzi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2019
  • Kodi Mungatani Kuti Muzisangalala Ndi Ntchito Yanu?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Galamukani!—2017
g17 No. 4 tsamba 2

Mawu Oyamba

Masiku ano, anthu ambiri amakhala otanganidwa moti mpaka nthawi zina sacheza ndi anzawo ngakhalenso anthu a m’banja lawo.

Ndiye kodi tingatani kuti tizigwiritsa ntchito bwino nthawi yathu?

Munthu wina wanzeru analemba kuti: “Kupuma pang’ono kuli bwino kuposa kugwira ntchito mwakhama ndi kuthamangitsa mphepo.”—Mlaliki 4:6.

Galamukani! iyi ikufotokoza mfundo zimene zingatithandize kuti tizigwiritsa ntchito nthawi mwanzeru komanso kuika zinthu zofunika pamalo oyamba.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena