Mawu Oyamba
N’chifukwa chiyani zinthu padzikoli zikuoneka ngati sizingayendenso bwino?
Baibulo limati: “Munthu amene akuyenda alibe ulamuliro wowongolera mapazi ake.”—Yeremiya 10:23.
“Galamukani!” iyi ikufotokoza chifukwa chake anthu ena amaona kuti zinthu padzikoli zidzakhala bwino kwambiri mtsogolo.