Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • hs tsamba 191
  • Mungapeze Buku Lina

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mungapeze Buku Lina
  • Mzimu Woyera—Mphamvu Yochirikiza Dongosolo Latsopano Likudza’lo!
  • Timitu
  • Mbiri Yabwino Yokusangalatsani
Mzimu Woyera—Mphamvu Yochirikiza Dongosolo Latsopano Likudza’lo!
hs tsamba 191

Mungapeze Buku Lina

Mbiri Yabwino Yokusangalatsani

Ife tonse timakonda mbiri yabwino, ndipo nali bukhu lathunthu lodzazidwa nayo! Bukhu lino limasimba m’kanenedwe kosabvuta chimene Baibulo limanena​—m’mene iro linaperekedwera ndi mbiri yabwino imene irimo. Bukhu’lo likuchirikizidwa ndi zithunzi-thunzi zoposa makumi asanu ndi limodzi. Iro lalinganizidwa kuthandiza anthu amene akufuna kudziwa zochuluka ponena za Baibulo, ponena za m’mene linalembedwera, kumene linachokera, chimene chiri uthenga wake. Bukhu la masamba 192 Mbiri Yabwino Yokusangalatsani limachita 40c yokha, litalipiriridwatu pa positi.

Mitengo ikhoza kusintha.

Lemberani ku Watchtower, mukumagwiritsira ntchito keyala iri yonse ya pa tsamba lotsatirapo’li.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena