Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • le tsamba 8
  • Kodi Imfa N’chiyani?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Imfa N’chiyani?
  • Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Tiyenera Kudziwa Zokhudza Angelo
    Zimene Baibulo Limaphunzitsa
  • Kodi Zochita za Angelo Ndiponso Ziwanda Zimakhudza Bwanji Anthufe?
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Kodi Anthu Akafa Amasanduka Angelo?
    Galamukani!—2006
  • Mmene Angelo Amatikhudzira
    Nsanja ya Olonda—2006
Onani Zambiri
Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
le tsamba 8

Kodi Imfa N’chiyani?

15 Pamene munthu afa, amabwerera ku fumbi. Sadziŵanso kanthu kali konse.—Salmo 146:4

Anthu akufa sangalankhule nanu kapena kuchita kanthu kali konse.—Mlaliki 9:5, 10

16 Koma angelo ambiri anakhala oipa. Tsopano iwo amayerekezera kukhala anthu amene anamwalira. Iwo amafuna kutipangitsa kukhulupirira kuti sitifa kwenikweni.—Genesis 6:1, 2; Yuda 6

17 Chotero Yehova Mulungu safuna kuti ife tikhulupirire angelo oipawo, otchedwa ziwanda.—Eksodo 22:18; Deuteronomo 18:10, 11; 32:17

Iye safuna kuti ife tichite kuombeza maula, ufiti kapena kumangirira zithumwa.—Agalatiya 5:19-21

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena