Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 17
  • “Mame” a Yehova Pakati pa Anthu Ambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mame” a Yehova Pakati pa Anthu Ambiri
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Achinyamata Ofanana ndi Mame Opatsa Mpumulo
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Kodi Utumiki Wanu Uli Ngati Mame?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Kodi Mumatsitsimula Ena?
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Mulungu Wachimwemwe, Anthu Achimwemwe!
    Nsanja ya Olonda—1987
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 17

Nyimbo 17

“Mame” a Yehova Pakati pa Anthu Ambiri

(Salmo 110:3)

1. Okongola ngati mame

Otsalira a Kristu.

Amamchititsatu kaso,

Posonkhana kwa iye.

2. Mkati mwa anthu ambiri,

Afanana ndi mame.

Atsitsimula ngofatsa.

Alondola mtendere.

3. Mabwenzi a otsalira

M’tsikuli Laufumu.

Nkhosa zina nzonga mame,

Zimatumikiranso.

4. Ambiri adzipereka,

Kumenyera Yehova.

Tikhaletu monga mame,

Polengeza Ufumu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena