Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 21
  • Tamandani Ufumu wa Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Ufumu wa Yehova!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
    Imbirani Yehova
  • Kugonjetsa Dziko
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo Yachilakiko
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 21

Nyimbo 21

Tamandani Ufumu wa Yehova!

(Chivumbulutso 11:17)

1. Akristunu tamandani

Ufumu wa Yehova,

Wokhazikitsidwa tsono

Ndi Mwana wake mmwamba.

Mikayeli agonjetsa

Satana ndi ziwanda.

Kristuyo adzatamanda

Mulungu m’dziko lonse.

2. Patsogolo “otsalira”

A “kagulu kankhosa”

Atamanda Ufumu wa

Mulungu wokwezedwa.

Oyembekezera dziko

Kukhala paradaiso

Thandizani “otsalira,”

Kulengeza Ufumu.

3. Tamani mosangalala!

Phunzitsani mwaluso;

Thandizani ofatsawo

Kukhala “’nthu abwino.”

Tamani Ufumu wake;

Bukitsani ubwino.

Udzadzetsa madalitso,

Ndi kulemekeza Ya.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena