Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 62
  • Achimwemwe, Ngachifundo!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Achimwemwe, Ngachifundo!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Anthu Achifundo Amakhala Odala
    Imbirani Yehova
  • ‘Atate Wanu Ndi Wachifundo’
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Timatumikira Mulungu “Wachifundo Chochuluka”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • “Osangalala Ndi Anthu Achifundo”
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 62

Nyimbo 62

Achimwemwe, Ngachifundo!

(Mateyu 5:7)

1. Achimwemwe ngachifundo!

Okongola kwa Mulungu.

Anena kwa abwinowo

M’lungu akonda chifundo.

Pa Kalivali Mulungu

Anakonza dipo lathu.

Adziŵa kufo’ka kwathu,

Ndi kusonyeza chifundo.

2. Odala ndi achifundo;

Akhulukidwa machimo.

Apindula mwachifundo

Kristu pokhala pampando.

Agaŵana chifundochi

Polalikira ponsepo,

Pouza anthu: “Kondwani

Chifukwa Ufumu wadza.”

3. Achifundo asawope

Chiweruzo cha Mulungu;

Adzasonyeza chifundo

Onse okhala m’chifundo.

O tikhale achifundo

Kusonyeza mkhalidwewo

Mwa kuchita nawo mwaŵi

Kutsanzira M’lungu wathu.

(MWALIZANI)

Achimwemwe ngachifundo! Okongola kwa Mulungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena