Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 98
  • Kumenyera Nkhondo Chikhulupiliro

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kumenyera Nkhondo Chikhulupiliro
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chikhulupiriro Chimatipatsa Mphamvu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Muzisonyeza Kuti Mumakhulupirira Malonjezo a Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Pitirizani Kulimbana ndi Zimene Zingakulepheretseni Kupeza Madalitso
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 98

Nyimbo 98

Kumenyera Nkhondo Chikhulupiliro

(Yuda 3)

1. Yesu ananeneratu,

Zoipa zachuluka.

Chikondi cha ochuluka;

Chakhala chozirala.

Chotero tilimbikire

Chikhulupilirocho

Cholandiridwa ndi mpingo

Wachikristu wakale.

2. Tisalole Satanayo

Kutifo’ketsa ife;

Koma tiime zolimba,

Mwantchito ndi pemphero.

Mwa kumenyabe nkhondoyo,

Sitidzawopa anthu,

Tidzalimbikitsanabe

Kuti tipiliretu.

3. Menyerani nkhondo zedi

Chikhulupilirocho.

Khalani mboni zolimba

Kufikira mapeto.

Mwa kuyeretsedwa kwa Ya

Kuipa kudzathadi,

Tidzawomboledwa ndithu

Mwa Teokrase wake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena