Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 104
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 104

Nyimbo 104

Nyimbo kwa Wammwambamwambayo

(Salmo 47:2)

1. Tiimbire Yehovayo;

Chitamandocho ndichake.

Mokondwa tiimbira Ya,

Tilengeza za mphamvu yake.

(Korasi)

2. Kondwa lipenga lilira:

Ufumu wa Ya wabadwa.

Khalidwe kwa Mpulumutsi,

Lisonye chiphunzitso chake.

(Korasi)

3. Tiri m’nthaŵi “zotsiriza”;

Tetezera kulambira.

Mulungu ngwachilakiko;

Tipereka thamo kwa iye.

(KORASi)

Yehova alamula;

Apeza chilakiko.

Ndi Mwanayo, Wofunika,

Ufumuwo wadza.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena