Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 151
  • Tilalikire Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tilalikire Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Ndi Ndani Amene Amalalikira Uthenga Wabwino?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova
  • “Lalika Mawu”!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 151

Nyimbo 151

Tilalikire Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu

(Mateyu 24:14)

1. Lalika Mbiri Yabwino ya Ufumu wa M’lungu.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

Polalika mbiriyi tikhale olimba mtima.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

Lalika mbiri pamakwalala ndi pamakomo;

Lalika mbiri yolembedwa kumitundu.

Lalika mwaluso, chifundo ndiponso mwachangu.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

2. Lalika madyererowo Yehova adzakonza.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

Kuti lidzakhala phwando logaŵira ofatsa.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

Lalika mbiri ya phwando la vinyo wosankhika,

Kuti onse anjala adzadye chakudya.

Kuti chipulumutso chikaŵalitsa pankhope.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

3. Lalika chisangalalo chomwe chidzakhalapo.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

Okonda Mawu a M’lungu sakhala ndi chisoni.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

Nenani pali thandizo kwa ochita chabwino,

Pali mtendere kwa odalira Mulungu.

Kutumikira Mulungu kuli kokondweretsa.

Tilalike mbiri ya Ufumu!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena