Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 160
  • Kuyenda Muumphumphu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuyenda Muumphumphu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yendani ndi Mtima Wosagawanika
    Imbirani Yehova
  • Kuchita Zinthu Mokhulupirika
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yendani mu Umphumphu
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 160

Nyimbo 160

Kuyenda Muumphumphu

(Salmo 26:1)

1. Weruzeni Yehova Mulungu.

Ndidalira inu ndiyenda mu’mphumphu.

Ndipendeni ndi kundiyesatu;

Mundiyeretsetu ndidalitsidwedi.

(Korasi)

2. Sindikhala ndi anthu oipa.

Ndimadana ndi onyoza chowonadi.

Musachotse moyotu wangawu,

Ndi anthu ochimwa odzala chiwawa.

(Korasi)

3. Munyumbayo ndikonda kukhala.

Kulambira kwanuko kuli kwangwiro.

Ndidzayenda kuguwa lanulo,

Kukutamandani padzikolonseli.

(KORASi)

Koma ine Ndatsimikizira

Kuti ndidzayenda Mu’mphumphu kosatha!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena