Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 185
  • Chiukiliro—Makonzedwe Achikondi a Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chiukiliro—Makonzedwe Achikondi a Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Phunziro 3
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Musawopa, Kagulu ka Nkhosa Inu”
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Ndi Kristu m’Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 185

Nyimbo 185

Chiukiliro—Makonzedwe Achikondi a Mulungu

(Yohane 11:25)

1. Chiukiliro chisonya

Chifundo cha M’lungu,

Chatsimikizidwa n’Kristu

M’chikondi cha M’lungu.

“Kagulu” kadzaukatu;

N’kukhala ndi moyo.

Popilira mpaka kufa,

Adzalamulira.

2. Moyo udzapatsidwanso

‘Kumtambo wa mboni.’

‘Chiukiliro chabwino’

Chalonjezedwatu.

Ngati “nkhosa zina” zifa

Zidzaukitsidwa

Kuchokera kumandako

Kudzatama M’lungu.

3. Onsewo okhala m’manda

Adzamvatu Yesu

Monga mbala yofa n’Yesu,

Adzakondwa m’moyo.

Potsiriza zaka chikwi,

Palitu chiyeso;

Amene adzapambana

Adzadalitsidwa.

4. O “otsalira” nonsenu

Ndi ‘nkhosa zinanu,’

Nenani akufa awo,

Adzawawonanso.

Chulukani muntchitozo

Mbuye walamula,

Poti mudziŵa imfayo

Singaletse mphotho.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena