Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 206
  • ‘Kondwerani m’Chiyembekezo’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Kondwerani m’Chiyembekezo’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Pitirizani Kulimbitsa Chiyembekezo Chanu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi Chiyembekezo Chodalirika Mungachipeze Kuti?
    Galamukani!—2004
  • Chiyembekezo—chinjirizo Lofunika m’Dziko Lopanda Chiyembekezo
    Nsanja ya Olonda—1993
  • Yembekezani Yehova Kuti Mukhale Olimba Mtima
    Nsanja ya Olonda—2006
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 206

Nyimbo 206

‘Kondwerani m’Chiyembekezo’

(Aroma 12:12)

1. Tiyamikira Mulungu

Ka’mba ka chiyembekezo.

Chiritu ngati nangula;

Chithandiza kupilira.

Chirinso ngati chisoti,

Chiletsa mivi kupyoza;

Chitichotsera zoipa

Chilimbitsa m’chilungamo.

2. Tikondwa m’chiyembekezo

Akufawo adzauka

Kuchoka kumanda awo

Kudzapanga paradaiso!

Inde, kunthaŵi zosatha

Adzakhalabe padziko

Adzapezatu chimwemwe,

M’makonzedwe a Mulungu.

3. M’chiyembekezo cholimba,

Tisachitetu choipa,

Koma kuphunzira Mawu

A M’lungu ndi kupemphera.

Kuti enanso akondwe,

Mwa dyera tisabisire,

Koma tidziŵitse iwo,

Kuti aime kwa M’lungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena