Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • gl tsamba 12-13
  • “Dziko Labwino ndi Lalikulu”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Dziko Labwino ndi Lalikulu”
  • ‘Onani Dziko Lokoma’
  • Nkhani Yofanana
  • Maphunziro Othandiza Otengedwa ku Dziko Lolonjezedwa
    Nsanja ya Olonda—1996
  • ‘Yendayenda M’dzikoli’
    Nsanja ya Olonda—2004
‘Onani Dziko Lokoma’
gl tsamba 12-13

“Dziko Labwino ndi Lalikulu”

PACHITSAMBA choyaka moto, Mulungu anauza Mose kuti Iye ‘adzalanditsa [anthu Ake] m’manja a Aigupto, ndi . . . kuwaloŵetsa m’dziko labwino ndi lalikulu, m’dziko moyenda mkaka ndi uchi ngati madzi.’—Eks. 3:8.

Kuona Dziko Lolonjezedwa Titalidula
Mmene Dzikolo Linalili

Zithunzi ziŵiri zili apazi zochita kupanga pakompyuta zingakuthandizeni kumvetsa zinthu zachilengedwe zosiyanasiyana za m’Dziko Lolonjezedwa ndi mmene deralo linalili. (Zithunzizi zakuzidwa kuti muthe kusiyanitsa bwinobwino mapiri, zigwa, nyanja, ndi mitsinje.) Pitani pa galafuyo ya tizigawo tamitundu yosiyanasiyana kuti muone kukwera kwa kumtunda poyerekeza ndi pamene pamalekeza madzi a nyanja zazikulu.

Tchati chikusonyeza njira ina yolongosolera mndandanda wa zinthu zachilengedwe m’dzikolo. M’Baibulo la Revised Nyanja (Union) Version, mawu akuti Araba ndi Shefela mwambiri anawamasulira kuti “kuchidikha,” pamene mawu akuti Negebu anawamasulira kuti “kum’mwera.”a—Gen. 13:1; Deut. 1:7; Yos. 11:16.

[Mawu a M’munsi]

a Mafotokozedwe ake ndi malemba ake a m’Baibulo a malowo mungawapeze mu buku la “All Scripture Is Inspired of God and Beneficial” (Study 1, masamba 270-8) ndi la Insight on the Scriptures (Voliyumu 2, masamba 568-71). Ofalitsidwa ndi Mboni za Yehova m’Chingelezi ndi zinenero zina zambiri.

[Tchati/Mapu patsamba 12, 13]

(Onani m’kabuku kenikeni kuti mumvetse izi)

Mmene Dzikolo Lilili

Tchati cha Zinthu Zachilengedwe

A. Gombe la Nyanja Yaikulu

B. Zidikha Kumadzulo kwa Yordano

1. Chidikha cha Aseri

2. Mkwasa wa Gombe la Doro

3. Mabusa a Saroni

4. Chidikha cha Filistiya

5. Chigwa Chapakati Chochokera Kum’maŵa Kupita Kumadzulo

a. Chidikha cha Megido

b. Chigwa cha Yezreeli

C. Mapiri Kumadzulo kwa Yordano

1. Mapiri a Galileya

2. Mapiri a Karimeli

3. Mapiri a Samariya

4. Shefela (zitunda)

5. Dera la Mapiri la Yuda

6. Chipululu cha Yuda

7. Negebu

8. Chipululu cha Parana

D. Araba (Chigwa)

1. Thamanda la Hula

2. Dera la Nyanja ya Galileya

3. Chigwa cha Yordano

4. Nyanja ya Mchere (Nyanja Yakufa)

5. Araba (kum’mwera kwa Nyanja ya Mchere)

E. Mapiri/Malo Okwera Kum’maŵa kwa Yordano

1. Basana

2. Gileadi

3. Amoni ndi Moabu

4. Dera la M’mapiri la Edomu

F. Mapiri a Lebano

[Map]

Phiri la Herimoni

Dani

Jerusalemu

Beere—seba

Kuona Dziko Lolonjezedwa Titalidula

mamita mafiti

2,500 7,500

2,000 6,000

1,500 4,500

1,000 3,000 Dera la Mapiri Dziko la

la Yuda Moabu

500 1,500

Shefela Chipululu

Chidikha cha Cha Yuda

Filistiya Rift

0 0 (Polekeza Madzi a Valley

Nyanja Zazikulu) Nyanja ya Mchere

-500 -1,500

[Chithunzi patsamba 13]

Phiri la Hermoni (2,814 m; 9,232 ft)

[Chithunzi patsamba 13]

Gombe la Nyanja ya Mchere; malo otsika kwambiri padziko lapansi (kuchoka polekeza madzi a nyanja zazikulu, lili pafupifupi mamita 400, mafiti 1,300 kutsika kupita pansi)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena