Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yp2 tsamba 216-217
  • Mtima Wanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mtima Wanu
  • Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Nchifukwa Ninji Kuli Kovuta Kwambiri Kuchotsa Maganizo Anga pa Osiyana Nawo Ziŵalo?
    Galamukani!—1994
  • Zimene Zinachitika Yesu Asanayambe Utumiki Wake
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
  • Kodi Ndingafotokoze Bwanji Zimene Ndimakhulupirira pa Nkhani ya Kugonana?
    Zimene Achinyamata Amafunsa
  • Ndingatani Kuti Ndisamangoganizira Zogonana?
    Zimene Achinyamata Amafunsa
Onani Zambiri
Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
yp2 tsamba 216-217

Chigawo 7

Mtima Wanu

Kodi mumaona kuti ndinu munthu wotani?

□ Wosachedwa kupsa mtima.

□ Wolephera ndiponso womangolakwitsa chilichonse.

□ Wongokhalira kudandaula.

□ Wongokhalira kuganiza za atsikana kapena anyamata.

□ Wofuna kugonana ndi atsikana kapena anyamata anzanga.

Ngati mwachonga chilichonse pa zinthu zimenezi, musataye mtima, chifukwa Mitu 26 mpaka 29 ikuthandizani pankhani zimenezi.

[Chithunzi chachikulu pamasamba 216, 217]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena