Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 84
  • “Ndikufuna”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndikufuna”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Ndifuna”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Ndikufuna”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Muziyenda Ndi Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yendani ndi Mulungu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 84

Nyimbo 84

“Ndikufuna”

Losindikizidwa

(Luka 5:13)

1. Anasonyeza chikondi

Pobweradi padzikoli.

Mwana wa Mulungu

Kukhala ndithu

Ndi anthu n’kuwaphunzitsa.

Anachiritsa odwala,

Akhungu ndi olumala.

Analitu wokhulupirika

Ananena: “Ndikufuna.”

2. Yehova watithandiza

Chifukwatu watipatsa

Mphatso ya Kapolo.

Tigwira ntchito

Nayetu mosangalala.

Ngati timakonda anthu

Iwo adzadziwiratu.

Choncho amasiye akapempha

Uwauze: “Ndikufuna.”

(Onaninso Yoh. 18:37; Aef. 3:19; Afil. 2:7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena