Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 14
  • Zinthu Zonse Zidzakhala Zatsopano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zinthu Zonse Zidzakhala Zatsopano
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Zinthu Zonse Zipangidwa Kukhala Zatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Zinthu Zonse Zimene Ndikupanga Ndi Zatsopano”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 14

Nyimbo 14

Zinthu Zonse Zidzakhala Zatsopano

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 21:1-5)

1. “Zizindikiro” zikusonyezadi

Kuti Yesu akulamulira.

Wapambana nkhondo ya kumwamba,

Posachedwa ayeretsa dziko.

(KOLASI)

Kondwa! Chifukwa Mulungu,

Alitu ndi anthu ake.

Sipadzakhalanso kulira,

Pena zopweteka ndi imfa;

Zidzakhala: ‘Zatsopano zonse.’

Mawuwa ndi oona.

2. Anthu aone Yerusalemuyo,

Mkwatibwi wa Mwanawankhosayo.

Atavala mochititsa chidwi,

Yehova ndiye kuwala kwake.

(KOLASI)

Kondwa! Chifukwa Mulungu,

Alitu ndi anthu ake.

Sipadzakhalanso kulira,

Pena zopweteka ndi imfa;

Zidzakhala: ‘Zatsopano zonse.’

Mawuwa ndi oona.

3. Mzindawu udzasangalatsa anthu.

Zipata zake sadzazitseka.

Anthu adzayenda muku’nika;

Atumikinu unikirani.

(KOLASI)

Kondwa! Chifukwa Mulungu,

Alitu ndi anthu ake.

Sipadzakhalanso kulira,

Pena zopweteka ndi imfa;

Zidzakhala: ‘Zatsopano zonse.’

Mawuwa ndi oona.

(Onaninso Mat. 16:3; Chiv. 12:7-9; 21:23-25.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena