Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 82
  • Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tikhale Ofatsa Ngati Khristu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ngachimwemwe Chotani Nanga Ofatsa!
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Yesetsani Kukhala Ofatsa Kuti Muzisangalatsa Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • ‘Kupeza Mpumulo wa Miyoyo Yanu’
    Nsanja ya Olonda—1989
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 82

Nyimbo 82

Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa

Losindikizidwa

(Mateyu 11:28-30)

1. Yesu anali woposa ’nthu onse.

Sanafune kutchuka, sananyade.

Anapatsidwa ntchito yofunika

Komabe anali wodzichepetsa.

2. Amene muli ndi mavuto nonse,

Goli lake akuti munyamule

Ndipo inu mudzatsitsimulidwa.

Ambuye wathu Yesu ndi wofatsa.

3. Anati: “Nonsenu ndinu abale.”

Musadzikweze, mutumikirane.

Ofatsa kwa M’lungu ndi ofunika,

Dziko lapansili adzalandira.

(Onaninso Mat. 5:5; 23:8; Miy. 3:34; Aroma 12:16.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena