Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 66
  • Tizitumikira Yehova ndi Moyo Wathu Wonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizitumikira Yehova ndi Moyo Wathu Wonse
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kutumikira Yehova Ndi Moyo Wonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Amayamikira Utumiki Wanu wa Mtima Wonse
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Mtundu Woyera wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 66

Nyimbo 66

Tizitumikira Yehova ndi Moyo Wathu Wonse

Losindikizidwa

(Mateyu 22:37)

1. Yehova Wamphamvuyonse

Inetu ndimakukondani.

Mtima wanga wonse umafuna

Kukutumikirani.

Malamulo anu ndimvera

Zofuna zanu ndichita.

(KOLASI)

Inu Yehova ndinu woyenera

Kutumikiridwa.

2. Atate, zomwe munalenga

Zimakulemekezani.

Ndadzipereka ndi mphamvu

Zonse kukutumikirani.

Zonse ndinakulonjezani

Ndidzayesetsa kuchita.

(KOLASI)

Inu Yehova ndinu woyenera

Kutumikiridwa.

(Onaninso Deut. 6:15; Sal. 40:8; 113:1-3; Mlal. 5:4; Yoh. 4:34.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena