Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 123
  • Abusa Ndi Mphatso za Amuna

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Abusa Ndi Mphatso za Amuna
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Abusa Ndi Mphatso
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Abusa Omwe Ndi ‘Zitsanzo kwa Gulu’ la Nkhosa
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Muzikonda Kwambiri Choonadi Panokha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 123

Nyimbo 123

Abusa Ndi Mphatso za Amuna

Losindikizidwa

(Aefeso 4:8)

1. Yehova amatithandiza

Kudzera mwa ’busa.

Mwa chitsanzo chawo chabwino

Amatsogolera.

(KOLASI)

Yehova watipatsa ’muna

Omwe tingadalire.

Amadera nkhawa za ife,

Ndiyetu tiwakonde.

2. Abusawa amatikonda,

Ndi okoma mtima.

Tikavulala amabwera

Kudzatichiritsa.

(KOLASI)

Yehova watipatsa ’muna

Omwe tingadalire.

Amadera nkhawa za ife,

Ndiyetu tiwakonde.

3. Safuna kuti tisochere,

Amatilangiza.

Kuti M’lungu tim’sangalatse

Pomutumikira.

(KOLASI)

Yehova watipatsa ’muna

Omwe tingadalire.

Amadera nkhawa za ife,

Ndiyetu tiwakonde.

(Onaninso Yes. 32:1, 2; Yer. 3:15; Yoh. 21:15-17; Mac. 20:28.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena