Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 5
  • Moyo wa Mpainiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Moyo wa Mpainiya
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 5

Nyimbo 140

Moyo wa Mpainiya

(Mlaliki 11:6)

  1. M’mawa uliwonse, tulo tisanathe,

    Timadzuka n’kupita

    kolalikira uthenga.

    Ndipo Mulungu amatitsogolera

    Timakondwa anthu

    akamamvetsera uthenga.

    (KOLASI)

    Tinasankha,

    kutumikira Yehova.

    Timachita zofuna zake.

    Tipitirizabe kulalikiraku,

    Tikatero timasonyeza

    Chikondi.

  2. Pofika madzulo, timatopa ndithu

    Komabe timapeza

    chimwemwe potumikira

    Madalitso Yehova amatipatsa

    Nthawi zonse

    timamuthokoza potithandiza.

    (KOLASI)

    Tinasankha,

    kutumikira Yehova.

    Timachita zofuna zake.

    Tipitirizabe kulalikiraku,

    Tikatero timasonyeza

    Chikondi.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 92:2; Aroma 14:⁠8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena