Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 9
  • Akamvera Adzapeza Moyo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Akamvera Adzapeza Moyo
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Akamvera Adzapeza Moyo
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 9

Nyimbo 144

Akamvera Adzapeza Moyo

(Ezekieli 3:17-19)

  1. Mulungu akufuna

    tichenjeze anthu

    Kuti tsiku la mkwiyo

    wake likubwera.

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza,

    Inde moyo wosatha

    Nafe tidzapulumuka,

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.

  2. Tili ndi uthenga

    woti tiuze anthu

    Tiitane anthu abwere

    kwa Mulungu

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza,

    Inde moyo wosatha

    Nafe tidzapulumuka,

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Mwamsanga tilengeze,

    Anthu amve, aphunzire.

    Cho’nadi tiphunzitse,

    Kuti moyo adzapeze.

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza,

    Inde moyo wosatha

    Nafe tidzapulumuka,

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.

(Onaninso 2 Mbiri 36:15; Yes. 61:2; Ezek. 33:6; 2 Ates. 1:⁠8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena