Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 13
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 13

Nyimbo 148

Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha

(Yohane 15:13)

  1. Yehova, tinali

    opanda tsogolo.

    Komano dipo

    lathandiza tonse.

    Tikudzipereka,

    kwa inu kosatha.

    Tiphunzitse ena,

    akudziweninso.

    (KOLASI)

    Mwana wanu yekha,

    munamupereka,

    Tidzakuimbirani,

    za mphatsoyi kwamuyaya.

  2. Chifundo chanucho

    ndi chachikuludi.

    Komanso timakonda

    dzina lanu.

    Yoposa zonsezi

    ndi mphatso ya Yesu.

    Anatifera kuti

    tipulumuke.

    (KOLASI)

    Mwana wanu yekha,

    munamupereka,

    Tidzakuimbirani,

    za mphatsoyi kwamuyaya.

    (KUMALIZA)

    Yehova, Atate, tikuthokozatu.

    Mphatsoyi munatipatsadi kwamuyaya.

(Onaninso Yoh. 3:16; 1 Yoh. 4:9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena