Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • lfb tsamba 240
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi N’chiyani Chimene Muyenera Kuchita?
    Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
  • Mfundo Zazikulu za Chigawo Chachitatu ndi Chachinayi cha Masalmo
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Gawo 4
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Zimene Zili M‘buku la Masalimo
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Onani Zambiri
Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
lfb tsamba 240

Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo

MUTU

Akufa adzaukitsidwa 48, 86, 91, 93

Ana inu, muzitumikira Yehova 37, 51, 59, 61, 72, 100

Kudzikonda kungachititse kuti ifeyo komanso anthu ena akumane ndi mavuto 3, 4, 12, 27, 28, 39, 49, 88

Kulambira konyenga kumachokera kwa Mdyerekezi 19, 20, 22, 38, 46, 49, 52, 58

Mkwiyo ndi woopsa 4, 12, 41, 45, 49, 65, 89

Muzikwaniritsa zimene mwalonjeza ngati mmene amachitira Yehova 8, 9, 11, 23, 24, 31, 34, 35, 36, 66, 93

Mulungu amadana ndi anthu oukira 7, 17, 26, 27, 28, 88

Musamachite zoipa 14, 27, 49, 53, 58, 88, 89

Musamataye mtima mukakumana ndi mavuto 16, 47, 51, 57, 64, 75, 90, 95, 99, 101

Musataye zimene Yehova wakupatsani 12, 13, 24, 35, 36, 56, 75, 95, 100

Muzikhululuka ngati Yehova 13, 15, 31, 43, 92

Muzimvera kuti mukhale ndi moyo 3, 5, 10, 37, 39, 54, 59, 65, 72

Muziyamika Yehova nthawi zonse 2, 6, 67, 103

Nsanje imadanitsa 4, 14, 41

N’zosatheka kukonda Mulungu ngati simukonda anzanu 4, 13, 15, 41

Oipa onse sadzakhalakonso 5, 10, 32, 46, 102

Simungatumikire Mulungu ndi chuma nthawi imodzi 10, 17, 44, 59, 75, 76

Tizigwirizana ndi anthu amene amakonda Yehova 16, 33, 42, 80, 87, 100, 103

Tizilalikira uthenga wabwino wa Ufumu 73, 76, 94, 95, 96, 97, 98

Tizimvera Yesu chifukwa ndi Mfumu ya Ufumu wa Mulungu 74, 78, 79, 83, 84, 85, 91, 92, 99

Ufumu wa Mulungu udzapangitsa kuti aliyense azikhala mosangalala 1, 48, 62, 79, 81, 83, 85, 86

Yehova adzatithandiza choncho tizichita zinthu molimba mtima 40, 47, 51, 53, 57, 61, 64, 65, 76, 88, 101

Yehova akhale mnzanu 11, 30, 33, 51, 56, 59, 69, 81, 82

Yehova amakonda anthu a mitundu yonse 30, 33, 48, 54, 77, 94, 97, 98, 99

Yehova amamvetsera tikamapemphera kuchokera mumtima 35, 38, 50, 64, 82

Yehova amaona kuti anthu onse ndi amtengo wapatali 8, 9, 11, 21, 23, 68, 70, 74, 87, 90

Yehova amateteza anthu amene amamukonda 6, 22, 40, 50, 52, 55, 64, 71, 84

Yehova amateteza anthu odzichepetsa 43, 45, 65, 67, 69

Yehova amatsogolera anthu ake 18, 25, 26, 27, 29, 34, 39, 44, 73, 80

Yehova analenga dziko kuti tizikhalamo 1, 2, 102, 103

Yehova anatipatsa Baibulo kuti litithandize kupeza nzeru 56, 66, 72, 75, 81

Yehova ndi Wamphamvuyonse 1, 7, 18, 19, 20, 21, 22, 26, 55, 60

Yehova saiwala zimene tamuchitira 16, 29, 32, 48, 65, 69, 77, 100

Yehova sanama 3, 10, 16, 63, 68, 70, 102, 103

Zimene Mulungu amafuna zidzachitika padzikoli ngati mmene zilili kumwamba 25, 55, 60, 62, 63, 71, 96, 102

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena