Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 7
  • Yehova Ndi Mphamvu Yathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Ndi Mphamvu Yathu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Ndiye Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova
  • Yehova, Nyonga Yathu ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ndipo Adzadziŵa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 7

NYIMBO 7

Yehova Ndi Mphamvu Yathu

Losindikizidwa

(Yesaya 12:2)

  1. 1. Yehova inu ndi mphamvu yathu.

    Inu ndinu Mpulumutsi wathu.

    Ndife Mboni za uthenga wanu,

    Anthu amve kapena akane.

    (KOLASI)

    Yehova ndinu mphamvudi yathu.

    Tilengezabe dzina lanu.

    Yehova ndinu wamphamvuyonse,

    M’lungu wathu ndinu thanthwe lathu.

  2. 2. Yehova mumatiwunikira

    Ndipo taphunzira choonadi.

    Malamulo anu tawadziwa.

    Ife tasankha Ufumu wanu.

    (KOLASI)

    Yehova ndinu mphamvudi yathu.

    Tilengezabe dzina lanu.

    Yehova ndinu wamphamvuyonse,

    M’lungu wathu ndinu thanthwe lathu.

  3. 3. Tizichita chifuniro chanu

    Ngakhale Satana atizunze.

    Tisafooke tithandizeni

    Kukhala kumbali yanu M’lungu.

    (KOLASI)

    Yehova ndinu mphamvudi yathu.

    Tilengezabe dzina lanu.

    Yehova ndinu wamphamvuyonse,

    M’lungu wathu ndinu thanthwe lathu.

(Onaninso 2 Sam. 22:3; Sal. 18:2; Yes. 43:12.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena