Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 11
  • Chilengedwe Chimatamanda Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chilengedwe Chimatamanda Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kumwamba Kumalengeza Ulemerero wa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Zakumwamba Zimalengeza Ulemerero wa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Pemphero Langa Losonyeza Kudzipereka
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Muziphunzira Zambiri Zokhudza Yehova Poona Chilengedwe Chake
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 11

NYIMBO 11

Chilengedwe Chimatamanda Mulungu

Losindikizidwa

(Salimo 19)

  1. 1. Munalenga chilengedwe chonse

    Ndipotu chimakutamandani.

    Ngakhale sichitulutsa mawu,

    Chimakutamandani Yehova.

    Ngakhale sichitulutsa mawu,

    Chimakutamandani Yehova. 

  2. 2. Anthu omwe amakuopani

    Adzapeza nzeru yeniyeni.

    Mfundo zanu zoposa golide

    N’zothandiza ana ndi akulu. 

    Mfundo zanu zoposa golide

    N’zothandiza ana ndi akulu.

  3. 3. Anthu omwe amakumverani

    Amakhala ndi moyo wabwino.

    Onse oyeretsa dzina lanu 

    Mudzawapatsatu madalitso.

    Onse oyeretsa dzina lanu 

    Mudzawapatsatu madalitso.

(Onaninso Sal. 12:6; 89:7; 144:3; Aroma 1:​20.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena