Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 19
  • Chakudya Chamadzulo cha Ambuye

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chakudya Chamadzulo cha Ambuye
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Mgonero wa Ambuye
    Imbirani Yehova
  • Chakudya Chamadzulo cha Ambuye
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 19

NYIMBO 19

Chakudya Chamadzulo cha Ambuye

Losindikizidwa

(Mateyu 26:​26-​30)

  1. 1. Yehova M’lungu wakumwamba,

    Lerotu ndi lapadera.

    Kale patsikuli munatisonyeza

    Chikondi, nzeru ndi mphamvu.

    Magazi a mwana wankhosa

    Anapulumutsa anthu,

    Kenako Yesu anakhetsa magazi

    Kukwaniritsa ulosiwu.

  2. 2. Tikuona mkate ndi vinyo

    Zomwe zikutikumbutsa

    Kufunika kwa Nsembe ya

    Yesu Khristu.

    Ndi mphatso yapaderadi.

    Madzulo ano tiyenera

    Kuchita chikumbutsochi

    Pokumbukira

    Zomwe zinachitika

    Kuti dipo liperekedwe.

  3. 3. Tasonkhana pamaso panu.

    Tamva kuitana kwanu.

    Titamande inu

    Ndi Mwana wanunso.

    Munatikonda kwambiri.

    Mwambowu ndi wolimbitsadi

    Chikhulupiriro chathu.

    Tiyendebe motsatira Yesu Khristu

    Ndipo tidzapezadi moyo.

(Onaninso Luka 22:​14-​20; 1 Akor. 11:​23-​26.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena