Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 57
  • Tizilalikira Anthu a Mitundu Yonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizilalikira Anthu a Mitundu Yonse
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tizilalikira kwa Anthu a Mitundu Yonse
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Mukhulupirikebe
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 57

NYIMBO 57

Tizilalikira Anthu a Mitundu Yonse

Losindikizidwa

(1 Timoteyo 2:4)

  1. 1. Timutsanzire Mulungu wathu

    Pokhala anthu opanda tsankho.

    Akufuna kuti anthu onse

    Amve uthenga, apulumuke.

    (KOLASI)

    Wofunika ndi munthu

    Osati mtundu wake.

    Tiphunzitse onse mosasankha.

    Timakondatu anthu,

    Tiwauze uthenga

    Akhale anzake a Yehova.

  2. 2. Kulikonse angapezekeko

    Kaya akuoneka motani,

    Mtima wawo ndiwo wofunika.

    Yehova amaona mtimawo.

    (KOLASI)

    Wofunika ndi munthu

    Osati mtundu wake.

    Tiphunzitse onse mosasankha.

    Timakondatu anthu,

    Tiwauze uthenga

    Akhale anzake a Yehova.

  3. 3. Yehova amalandira anthu

    Omwe asankha kum’tumikira.

    Choncho anthu a mitundu yonse,

    Tiwauze uthenga wabwino.

    (KOLASI)

    Wofunika ndi munthu

    Osati mtundu wake.

    Tiphunzitse onse mosasankha.

    Timakondatu anthu,

    Tiwauze uthenga

    Akhale anzake a Yehova.

(Onaninso Yoh. 12:32; Mac. 10:34; 1 Tim. 4:​10; Tito 2:​11.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena