Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 91
  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
  • “Talawani Ndipo Muona Kuti Yehova Ndi Wabwino”
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 91

NYIMBO 91

Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi

Losindikizidwa

(Salimo 127:1)

  1. 1. Yehova tikufuna

    Kupemphera mothokoza

    Chifukwa mwatikonda

    Potipatsa nyumbayi.

    Taona mwadalitsa

    Ntchito imene tagwira

    Ndipo taimanga chifukwa

    Mwatithandiza.

    (KOLASI)

    Kukumangirani nyumbayi

    Yehova unali mwayi.

    Tilemekeze dzina lanu nthawi zonse

    Ndi kukutumikirani.

  2. 2. Ndife osangalala

    Kuti tapeza anzathu.

    Sitidzaiwala mpakana

    M’Paradaiso.

    Taona mzimu wanu

    Chifukwa chogwirizana.

    Uwu unali mwayi wokweza

    Dzina lanu.

    (KOLASI)

    Kukumangirani nyumbayi

    Yehova unali mwayi.

    Tilemekeze dzina lanu nthawi zonse

    Ndi kukutumikirani.

(Onaninso Sal. 116:1; 147:1; Aroma 15:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena