Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 92
  • Malo Odziwika Ndi Dzina Lanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Malo Odziwika Ndi Dzina Lanu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Malo Odziwika ndi Dzina Lanu
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 92

NYIMBO 92

Malo Odziwika Ndi Dzina Lanu

Losindikizidwa

(1 Mbiri 29:16)

  1. 1. Yehova tinali ndi mwayi

    Okumangirani nyumba.

    Tikukupatsani tsopano.

    Dzina lanu lidziwike.

    Zonse zomwe timapereka

    Zimakhala zanu zomwe.

    Luso, mphamvu ndi chuma chathu,

    Tazipereka kwa inu.

    (KOLASI)

    Tikupereka malowa

    Kuti mudziwikedi.

    Tikupereka malowa,

    Chonde alandireni.

  2. 2. Tikulemekeza inuyo

    Pokutamandani pano.

    Landirani ulemerero

    Tikamachuluka muno.

    Malowa tikukupatsani

    Ndipo tiziwasamala,

    Kuti apereke umboni

    Za dzina lanu loyera.

    (KOLASI)

    Tikupereka malowa

    Kuti mudziwikedi.

    Tikupereka malowa,

    Chonde alandireni.

(Onaninso 1 Maf. 8:​18, 27; 1 Mbiri 29:​11-14; Mac. 20:24.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena