Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 101
  • Tizichita Zinthu Mogwirizana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizichita Zinthu Mogwirizana
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tigwire Ntchito Mogwirizana
    Imbirani Yehova
  • Kugwirira Ntchito Pamodzi m’Chigwirizano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Banja la Yehova Lili ndi Umodzi Wamtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Akhristu Oona Amadziwika Chifukwa cha Kugwirizana
    Nsanja ya Olonda—2010
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 101

NYIMBO 101

Tizichita Zinthu Mogwirizana

Losindikizidwa

(Aefeso 4:3)

  1. 1. M’dziko logawikanali,

    Tili m’gulu la Mulungu.

    Timakhala mwamtendere,

    Timasangalala.

    Timaunyadira

    Mgwirizanowu.

    Tili ndi ntchito yambiri.

    Yesu akutsogolera.

    Tiyeni tizimumvera

    N’kumagwirizana.

  2. 2. Popempherera umodzi

    Tizikondana kwambiri.

    Chikondi chimabweretsa

    Chimwemwe, mtendere.

    Mgwirizano wathu

    Ndi wabwinodi.

    Pamene tikukondana,

    M’lungu adzatithandiza

    Kukhala ogwirizana,

    Pomutumikira.

(Onaninso Mika 2:12; Zef. 3:9; 1 Akor. 1:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena