Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 105
  • “Mulungu Ndi Chikondi”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mulungu Ndi Chikondi”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova
  • Tanthauzo la Kukonda Mnansi Wathu
    Nsanja ya Olonda—2006
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
  • Kondani Mulungu Amene Amakukondani
    Nsanja ya Olonda—2006
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 105

NYIMBO 105

“Mulungu Ndi Chikondi”

Losindikizidwa

(1 Yohane 4:​7, 8)

  1. 1. Mulungu ndi wachikondi ndiye

    Tiyende naye.

    Tikonde M’lungu ndi anthu.

    Tizichita zabwino.

    Tidzasangalala ndithu,

    Tidzapezanso moyo.

    Tizisonyeza chikondi

    Ngati cha Yesu Khristu.

  2. 2. Tikakonda choonadi

    Tidzachita zabwino.

    Tikalakwitsa ndi kugwa

    M’lungu amatidzutsa.

    Chikondi chilibe nsanje

    Ndipo chimapirira.

    Tikamakonda anzathu

    Tidzadalitsidwadi.

  3. 3. Musalole kuti mkwiyo

    Ukulamulireni.

    Khulupirirani M’lungu,

    Adzakuphunzitsani

    Kukonda M’lungu ndi anthu.

    N’chikondi chenicheni.

    Tizisonyeza anzathu

    Chikondi cha Mulungu.

(Onaninso Maliko 12:​30, 31; 1 Akor. 12:31–​13:8; 1 Yoh. 3:​23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena