Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 107
  • Tizitsanzira Chikondi cha Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizitsanzira Chikondi cha Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
  • Chikondi Ndi Khalidwe Lamtengo Wapatali Kwambiri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kondani Mulungu Amene Amakukondani
    Nsanja ya Olonda—2006
  • ‘Chachikulu cha Izi Ndicho Chikondi’
    Nsanja ya Olonda​—1990
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 107

NYIMBO 107

Tizitsanzira Chikondi cha Mulungu

Losindikizidwa

(1 Yohane 4:19)

  1. 1. Yehova M’lungu n’chitsanzo chabwino,

    Inde cha chikondi.

    Zochita zake zimatithandiza

    Kuti tizimutsanzira.

    Anatipatsa mwana wake Yesu

    Kuti tikhululukidwe zolakwa.

    Ndi umbonidi wa chikondi chake.

    M’lungu wathu ndi chikondidi.

  2. 2. Timasonyeza chikondi choona

    Potsanzira M’lungu.

    Abale onse timawathandiza

    Mosasankha aliyense.

    Chikondi chingakhale chenicheni

    Ngati timakonda M’lungu ndi anthu.

    Tizikwirira zolakwa za ena,

    Chimenechi ndicho chikondi.

  3. 3. Chikondi chathu chimatithandiza

    Kumagwirizana.

    Atate wathu akufuna kuti

    Tidzalawe mgwirizano.

    Timapeza chikondi chenicheni

    Ndipo n’chomwe chimatidziwikitsa.

    Abale athu amatikumbutsa

    Za chikondi cha M’lungu wathu.

(Onaninso Aroma 12:10; Aef. 4:3; 2 Pet. 1:7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena