Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 110
  • “Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka
    Imbirani Yehova
  • Chimwemwe cha Yehova Ndicho Linga Lathu
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 110

NYIMBO 110

“Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka”

Losindikizidwa

(Nehemiya 8:10)

  1. 1. Zizindikiro zasonyeza kuti

    Ufumu wayandikira.

    Chipulumutso chayandikiradi.

    Tukulani mitu yanu.

    (KOLASI)

    Chimwemwe chochoka kwa Yehova

    Ndi malo achitetezo.

    Imbani mofuula ndi chimwemwe

    Chifukwa cha chiyembekezo.

    Chimwemwe chochoka kwa Yehova

    Ndi malo achitetezo.

    Tilambire M’lungu modzipereka.

    Tim’tumikire mwachimwemwe.

  2. 2. Inu nonse okondadi Yehova

    Muzimukhulupirira.

    Imirirani ndipo fuulani.

    Imbani mosangalala.

    (KOLASI)

    Chimwemwe chochoka kwa Yehova

    Ndi malo achitetezo.

    Imbani mofuula ndi chimwemwe

    Chifukwa cha chiyembekezo.

    Chimwemwe chochoka kwa Yehova

    Ndi malo achitetezo.

    Tilambire M’lungu modzipereka.

    Tim’tumikire mwachimwemwe.

(Onaninso 1 Mbiri 16:27; Sal. 112:4; Luka 21:28; Yoh. 8:32.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena