Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 116
  • Kukoma Mtima Ndi Kofunika Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukoma Mtima Ndi Kofunika Kwambiri
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Lofunika Kwambiri
    Imbirani Yehova
  • Kukoma Mtima Ndi khalidwe Limene Limasonyezedwa M’mawu ndi Zochita
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Anthu a Mulungu Ayenera Kukonda Khalidwe la Kukoma Mtima
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Mkondweretseni Yehova Mwakusonyeza Kukoma Mtima
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 116

NYIMBO 116

Kukoma Mtima Ndi Kofunika Kwambiri

Losindikizidwa

(Aefeso 4:​32)

  1. 1. Tikukutamandani Yehova,

    Mwatipatsa Mawu.

    Taona nzeru zanu zakuya

    Ndi kukoma mtima kwanu.

  2. 2. Yesu akuuza ovutika

    Apite kwa iye.

    Akanyamule goli lakelo

    Kuti atsitsimulidwe.

  3. 3. Mulungu wathu ndi Mwana wake

    Ndi okoma mtima.

    Nafe tikhale okoma mtima.

    Tizilimbikitsa ena.

(Onaninso Mika 6:8; Mat. 11:​28-​30; Akol. 3:​12; 1 Pet. 2:3.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena