Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 118
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Imbirani Yehova
  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
    Imbirani Yehova
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 118

NYIMBO 118

“Tiwonjezereni Chikhulupiriro”

Losindikizidwa

(Luka 17:5)

  1. 1. Yehova ndifedi anthu ochimwa,

    Mtima wathu umatipusitsa.

    Pali tchimo lomwe limatikola,

    Kuchepa kwa chikhulupiriro.

    (KOLASI)

    Mulungu wathu tiwonjezereni

    Chikhulupiriro chilimbedi.

    Mwa chifundo chanu mutithandize

    Tikulemekezeni mu zonse.

  2. 2. Ngati sitikukhulupirirani

    Sitingakusangalatsenidi.

    Chikhulupiriro chimateteza

    Ndipo chimatilimbitsa mtima.

    (KOLASI)

    Mulungu wathu tiwonjezereni

    Chikhulupiriro chilimbedi.

    Mwa chifundo chanu mutithandize

    Tikulemekezeni mu zonse.

(Onaninso Gen. 8:21; Aheb. 11:6; 12:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena