Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CA-brpgm17 tsamba 3-4
  • Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Otsatirawa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Otsatirawa
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wadera ya 2016-2017—Wokhala ndi Woimira Nthambi
  • Nkhani Yofanana
  • Kondani Mulungu Amene Amakukondani
    Nsanja ya Olonda—2006
  • “Mupitirize Kukonda Abale”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Zimene Tingaphunzire Kwa “Wophunzira Amene Yesu Anali Kumukonda Kwambiri”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • “Uzikonda Yehova Mulungu Wako”
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wadera ya 2016-2017—Wokhala ndi Woimira Nthambi
CA-brpgm17 tsamba 3-4

Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Otsatirawa:

  1. Kodi lamulo lalikulu kwambiri ndi liti, nanga ndi lofunika bwanji? (Mat. 22:37, 38; Maliko 12:30)

  2. Kodi tingapewe bwanji kukonda dziko? (1 Yoh. 2:15-17)

  3. Kodi tingaphunzitse bwanji anthu ena kuti ‘azikonda dzina la Yehova’? (Yes. 56:6, 7)

  4. Kodi tingasonyeze bwanji kuti timakonda abale athu mopanda chinyengo? (1 Yoh. 4:21)

  5. Kodi makolo angaphunzitse bwanji ana awo kuti azikonda Yehova? (Deut. 6:4-9)

  6. Kodi mungatani kuti Yehova akhale mnzanu wapamtima? (1 Yoh. 5:3)

  7. Kodi tingatani kuti tisasiye kapena tiyambirenso kukonda Yehova? (Chiv. 2:4, 5)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena