Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • rr tsamba 88-89
  • Maulosi Atatu Okhudza Mesiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Maulosi Atatu Okhudza Mesiya
  • Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • 1. “Amene Ali Woyenerera Mwalamulo” (Ezekieli 21:25-27)
  • 2. “Mtumiki Wanga . . . Adzawadyetsa Komanso Adzakhala M’busa Wawo” (Ezekieli 34:22-24)
  • 3. “Onsewo Adzalamuliridwa ndi Mfumu Imodzi” Mpaka Kalekale (Ezekieli 37:22, 24-28)
  • “Ndidzazipatsa Mʼbusa Mmodzi”
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Mmene Mungapezere Malemba M’Baibulo Lanu
    Nkhani Zina
  • Chaka cha 1914 Ndi Chaka Chapadera Kwambiri
    Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?
  • Kodi Ufumu Umene Walamulira kwa Zaka 100 Umakukhudzani Bwanji?
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
rr tsamba 88-89

BOKOSI 8B

Maulosi Atatu Okhudza Mesiya

Losindikizidwa

1. “Amene Ali Woyenerera Mwalamulo” (Ezekieli 21:25-27)

NTHAWI ZA ANTHU AKUNJA (607 B.C.E.–1914 C.E.)

  1. 607 B.C.E.​—Zedekiya anachotsedwa pa ufumu

  2. 1914 C.E.​—Yesu amene ndi “woyenerera mwalamulo” kukhala Mfumu komanso Mesiya anaikidwa kukhala Mfumu ndipo anakhala M’busa ndiponso Wolamulira

Bwererani ku mutu 8, ndime 12-15

2. “Mtumiki Wanga . . . Adzawadyetsa Komanso Adzakhala M’busa Wawo” (Ezekieli 34:22-24)

MASIKU OTSIRIZA (1914 C.E.–PAMBUYO PA ARAMAGEDO)

  1. 1914 C.E.​—Yesu amene ndi “woyenerera mwalamulo” kukhala Mfumu komanso Mesiya anaikidwa kukhala Mfumu ndipo anakhala M’busa ndiponso Wolamulira

  2. 1919 C.E.​—Kapolo wokhulupirika komanso wanzeru anasankhidwa kuti aziweta nkhosa za Mulungu

    Akhristu odzozedwa okhulupirika anasonkhanitsidwa pamodzi ndi Mesiya yemwenso ndi Mfumu, ndipo kenako anakhala gulu limodzi ndi a khamu lalikulu

  3. PAMBUYO PA ARAMAGEDO​—Madalitso amene adzakhalepo Mfumu ikamadzalamulira adzakhalapo mpaka kalekale

Bwererani ku mutu 8, ndime 18-22

3. “Onsewo Adzalamuliridwa ndi Mfumu Imodzi” Mpaka Kalekale (Ezekieli 37:22, 24-28)

MASIKU OTSIRIZA (1914 C.E.–PAMBUYO PA ARAMAGEDO)

  1. 1914 C.E.​—Yesu amene ndi “woyenerera mwalamulo” kukhala Mfumu komanso Mesiya anaikidwa kukhala Mfumu ndipo anakhala M’busa ndiponso Wolamulira

  2. 1919 C.E.​—Kapolo wokhulupirika komanso wanzeru anasankhidwa kuti aziweta nkhosa za Mulungu

    Akhristu odzozedwa okhulupirika anasonkhanitsidwa pamodzi ndi Mesiya yemwenso ndi Mfumu, ndipo kenako anakhala gulu limodzi ndi a khamu lalikulu

  3. PAMBUYO PA ARAMAGEDO​—Madalitso amene adzakhalepo Mfumu ikamadzalamulira adzakhalapo mpaka kalekale

Bwererani ku mutu 8, ndime 23-26

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena