Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm23 tsamba 2-8
  • Lachisanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lachisanu
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2023
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Masana
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2023
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2023
CO-pgm23 tsamba 2-8
Zithunzi: Zina zomwe zili mupulogalamu ya Lachisanu. 1. Mfumu Sauli ikulowa m’phanga limene Davide pamodzi ndi amuna omwe ali nawo abisalamo. 2. Banja lili mu utumiki. 3. Mbalame zili ndi ana awo

Penguins: By courtesy of John R. Peiniger

Lachisanu

“Chikondi n’choleza mtima” 1 Akorinto 13:4

M’Mawa

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 66 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YA TCHEYAMANI: N’chifukwa Chiyani Tiyenera ‘Kukhala Oleza Mtima’? (Yakobo 5:7, 8; Akolose 1:9-11; 3:12)

  • 10:10 NKHANI YOSIYIRANA: “Chilichonse Chili ndi Nthawi Yake”

    • • Muziganizira Mmene Yehova Amaonera Nthawi (Mlaliki 3:1-8, 11)

    • • Kulimbitsa Ubwenzi ndi Anzathu Kumatenga Nthawi (Miyambo 17:17)

    • • Kukula Mwauzimu Kumatenga Nthawi (Maliko 4:26-29)

    • • Kukwaniritsa Zolinga Kumatenga Nthawi (Mlaliki 11:4, 6)

  • 11:05 Nyimbo Na. 143 ndi Zilengezo

  • 11:15 KUWERENGA BAIBULO MWASEWERO: Davide Anayembekezera Yehova (1 Samueli 24:2-15; 25:1-35; 26:2-12; Salimo 37:1-7)

  • 11:45 Muzisangalala ndi Kuleza Mtima kwa Mulungu (Aroma 2:4, 6, 7; 2 Petulo 3:8, 9; Chivumbulutso 11:18)

  • 12:15 Nyimbo Na. 147 ndi Kupuma

Masana

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 17

  • 1:50 Muzitsanzira Kuleza Mtima kwa Yesu (Aheberi 12:2, 3)

  • 2:10 NKHANI YOSIYIRANA: Muzitsanzira Anthu Amene Anadalitsidwa Chifukwa cha Kuleza Mtima

    • • Abulahamu ndi Sara (Aheberi 6:12)

    • • Yosefe (Genesis 39:7-9)

    • • Yobu (Yakobo 5:11)

    • • Moredekai ndi Esitere (Esitere 4:11-16)

    • • Zekariya ndi Elizabeti (Luka 1:6, 7)

    • • Paulo (Machitidwe 14:21, 22)

  • 3:10 Nyimbo Na. 11 ndi Zilengezo

  • 3:20 NKHANI YOSIYIRANA: Zimene Chilengedwe Chimatiphunzitsa Zokhudza Mmene Yehova Amaonera Nthawi

    • • Zomera (Mateyu 24:32, 33)

    • • Zolengedwa za M’madzi (2 Akorinto 6:2)

    • • Mbalame (Yeremiya 8:7)

    • • Tizilombo (Miyambo 6:6-8; 1 Akorinto 9:26)

    • • Nyama Zapamtunda (Mlaliki 4:6; Afilipi 1:9, 10)

  • 4:20 “Simukudziwa Tsiku Kapena Ola Lake” (Mateyu 24:36; 25:13, 46)

  • 4:55 Nyimbo Na. 27 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena