Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w87 8/15 tsamba 24
  • Mtanda Wachikristu Asanafike Constantine?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mtanda Wachikristu Asanafike Constantine?
  • Nsanja ya Olonda—1987
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mtanda Uli wa Akristu?
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Chimene Chikondi cha Mulungu Chimatanthauza
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Mtanda
    Kukambitsirana za m’Malemba
  • Kodi N’zoona Kuti Yesu Anafera Pamtanda?
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—1987
w87 8/15 tsamba 24

Mtanda Wachikristu Asanafike Constantine?

”CHIZINDIKIRO cha mtanda chakhala chizindikiro cha zinthu zakale kwambiri, chopezeka chifupifupi mu miyambo iriyonse yodziwika. Tanthauzo lake lachititsa kakasi akatswiri odziwa za mafuko a anthu, ngakhale kuti kugwiritsiridwa ntchito kwake kwa mu zaluso zosonyeza maliro modziwika bwino kungaloze ku kuchinjiriza molimbana ndi choipa. Kumbali ina, crux ansata yotchuka ya ku Igupto, yosonyezedwa kukhala ikuchokera mkamwa, iyenera kulozera ku moyo kapena mpweya. Kugwiritsiridwa ntchito kwa dziko lonse kwa chizindikiro cha mtanda kumamveketsa maganizo kwambiri kusoweka kowonekera kwa mitanda mu zotsalira za Chikristu choyambirira, makamaka chisonyezero chachindunji chirichonse ku chochitika cha pa Golgota. Ophunzira ambiri tsopano amavomereza kuti mtanda, monga cholozera cha luso ku chochitika cha chikondi, sungapezeke kumayambiriro nthawi ya Constantine isanadze.”​—Ante Pacem—​Archaeological Evidence of Church Life Before Constantine (1985), ya Professor Graydon F. Snyder, tsamba 27.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena