Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 5/1 tsamba 24-25
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Nkhani Yofanana
  • Phunziro 2
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Anthu 8 Anapulumuka
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Nowa Akhoma Chingalawa
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • “Nowa Anayenda ndi Mulungu Woona”
    Nsanja ya Olonda—2013
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—2012
w12 5/1 tsamba 24-25

Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo

ANA AZAKA ZOSAPITIRIRA ZITATU

Ona nyama zimene zili pafupi ndi chingalawa cha Nowa.

Kodi ndi nyama ziti zimene zimalira ngati ng’ombe? Nanga ndi ziti zimene zimauwa?

Chingalawa cha Nowa chinapulumutsa nyama zonse, zazifupi ndi zazitali. Genesis 7:7-10; 8:15-17

ZOTI MAKOLO ACHITE

Muuzeni mwana wanuyo kuti aloze:

Chingalawa

Chimbalangondo

Galu

Njovu

Kadyamsonga

Mkango

Nyani

Nkhumba

Nkhosa

Mbidzi

Utawaleza

Mtengo

Kodi ungathe kuyerekeza mmene nyama izi zimalirira?

Galu

Mkango

Nyani

Nkhumba

Nkhosa

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena