Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 6/15 tsamba 12-13
  • Yehova Anaulula Mafumu 8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Anaulula Mafumu 8
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Ndi “Woulula Zinsinsi”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Yehova Waulula “Zimene Ziyenera Kuchitika Posachedwapa”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Zimene Zili M’buku la Chivumbulutso Zimakhudzanso Adani a Mulungu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kulimbana ndi Zilombo Ziwiri Zoopsa
    Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—2012
w12 6/15 tsamba 12-13

Yehova Anaulula Mafumu 8

Mabuku a m’Baibulo a Danieli ndiponso Chivumbulutso amaulula mafumu 8, kapena kuti maulamuliro 8 a anthu. Amasonyezanso nthawi imene maulamulirowo adzaonekera. Kumvetsa ulosi woyambirira wa m’Baibulo kungatithandize kumvetsanso maulosi a m’buku la Danieli ndiponso Chivumbulutso amenewa.

Kuyambira kalekale, Satana anakonza zoti mbewu yake izikhala ndi maufumu kapena maboma. (Luka 4:5, 6) Koma ndi maufumu ochepa okha padziko lapansi amene alowerera kwambiri m’zochita za anthu a Mulungu, omwe ndi Aisiraeli ndiponso Akhristu odzozedwa. Masomphenya a Danieli ndi Yohane amafotokoza maulamuliro 8 okha amene achita zimenezi.

[Tchati/​Zithunzi pamasamba 12, 13]

(Onani m’magazini yeniyeni kuti mumvetse izi)

MAULOSI A MAULOSI A M’BUKU

M’BUKU LA DANIELI LA CHIVUMBULUTSO

1. Iguputo

2. Asuri

3. Babulo

4. Mediya ndi

Perisiya

5. Girisi

6. Roma

7. Britain ndi

United Statesa

8. Mabungwe a League of Nations

ndi United Nationsb

ANTHU A MULUNGU

2000 B.C.E.

Abulahamu

1500

Mtundu wa Isiraeli

1000

Danieli 500

B.C.E./​C.E.

Yohane

Isiraeli wa Mulungu 500

1000

1500

2000 C.E.

[Mawu a M’munsi]

a Mafumu onsewa akhalapo nthawi ya mapeto. Onani tsamba 19.

b Mafumu onsewa akhalapo nthawi ya mapeto. Onani tsamba 20.

[Zithunzi]

Chifaniziro chachikulu (Dan. 2:31-45)

Zilombo zinayi zimene zinatuluka m’nyanja (Dan. 7:3-8, 17, 25)

Nkhosa yamphongo ndi mbuzi (Dan. 8)

Chilombo cha mitu 7 (Chiv. 13:1-10, 16-18)

Chilombo cha nyanga ziwiri chinalimbikitsa anthu kupanga chifaniziro cha chilombo (Chiv. 13:11-15)

[Mawu a Zithunzi]

Photo credits: Egypt and Rome: Photograph taken by courtesy of the British Museum; Medo-Persia: Musée du Louvre, Paris

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena