Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 January tsamba 3
  • Tizichita Khama Polambira Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizichita Khama Polambira Yehova
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Anatipatsa Ufulu Wosankha
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Chitsanzo Chabwino—Hezekiya
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • “Anapitiriza Kumamatira Yehova”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Mulungu Athandiza Mfumu Hezekiya
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 January tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 MBIRI 29-32

Tizichita Khama Polambira Yehova

Losindikizidwa
Kachisi wa Solomo ku Yerusalemu

Hezekiya anathandiza anthu kuti ayambenso kulambira Yehova

29:10-17

  • 746-716 B.C.E.

    Hezekiya Analamulira Kuyambira mu

  • NISANI 746 B.C.E.

    • Tsiku loyamba mpaka la 8: Anayeretsa Bwalo la Mkati

    • Tsiku la 9 mpaka la 16: Anayeretsa Nyumba ya Yehova

    • Anapereka nsembe yophimba machimo a Aisiraeli onse ndipo anthu anayambanso kulambira Mulungu

  • 740 B.C.E.

    Mzinda wa Samariya Unawonongedwa

Hezekiya anasonkhanitsa anthu kuti alambire Yehova

30:5, 6, 10-12

  • Anthu anatumidwa kukapereka makalata olengeza za Pasika. Anapereka makalatawa kuyambira ku Beere-seba mpaka ku Dani

  • Ena ananyozera uthengawo koma ena anamvera

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena