Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 January tsamba 7
  • Yehova Amafuna Kuti Tizimutumikira ndi Mtima Wonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amafuna Kuti Tizimutumikira ndi Mtima Wonse
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Ezara
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Ezara Ankaphunzitsa Chilamulo cha Mulungu
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Mukhoza Kukhalabe Olimba Mtima pa Nthawi Yovuta
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Kodi Mumaphunzitsa Zogwira Mtima?
    Nsanja ya Olonda—2002
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 January tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EZARA 6-10

Yehova Amafuna Kuti Tizimutumikira ndi Mtima Wonse

Losindikizidwa
Ayuda akuchoka ku Babulo kupita ku Yerusalemu limodzi ndi Ezara

Ezara anakonzekera kubwerera ku Yerusalemu

7:6, 22; 8:26, 27

  • Ezara analoledwa ndi Mfumu Aritasasita kuti apite ku Yerusalemu kukathandiza anthu kuti azilambira Yehova

  • Mfumu inapatsa Ezara “zopempha zake zonse” kuti akamangire nyumba ya Yehova. Inamupatsa golide, siliva, tirigu, vinyo, mafuta ndi mchere. Malinga ndi ndalama za masiku ano, zonse zingakwane madola 100 miliyoni a ku America

Ezara ankakhulupirira kuti Yehova ateteza atumiki ake

7:13; 8:21-23

  • Ulendo wobwerera ku Yerusalemu unali wovuta

  • Unali mtunda wa makilomita pafupifupi 1,600 ndipo ankadutsa m’malo oopsa

  • Ulendowu unatenga miyezi pafupifupi 4

  • Anthu obwererawo anafunika kukhala ndi chikhulupiriro champhamvu, kulimba mtima komanso kukonda kwambiri kulambira Yehova

EZARA ANATENGA . . .

Golide ndi siliva zolemera matalente oposa 750

MAVUTO AMENE ANTHU ANAKUMANA NAWO POBWERERA . . .

Magulu a zigawenga, kutentha kwa m’chipululu, zilombo zolusa

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena