Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 May tsamba 7
  • Tizidalira Yehova Kuti Tikhale Olimba Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizidalira Yehova Kuti Tikhale Olimba Mtima
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Davide Sankachita Mantha
    Phunzitsani Ana Anu
  • “Yehova Ndiye Mwini Nkhondo”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2016
  • “Ndiphunzitseni Kuchita Chifuniro Chanu”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • ‘Limba Mtima Ndipo Ugwire Ntchitoyi’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 May tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 26-33

Tizidalira Yehova Kuti Tikhale Olimba Mtima

Davide analimba mtima chifukwa chokumbukira mmene Yehova anamupulumutsira

27:1-3

  • Yehova anapulumutsa Davide kwa mkango

  • Yehova anathandiza Davide kupha chimbalangondo kuti ateteze nkhosa

  • Yehova anathandiza Davide kupha Goliyati

Davide akukumbukira mmene Yehova anamupulumutsira kwa mkango, mmene anamuthandizira kupha chimbalangondo komanso mmene anamuthandizira kupha Goliyati

Kodi n’chiyani chingatithandize kukhala olimba mtima ngati Davide?

27:4, 7, 11

  • Pemphero

  • Kulalikira

  • Kupezeka pamisonkhano

  • Kuphunzira Baibulo patokha komanso kulambira kwa pabanja

  • Kulimbikitsa ena

  • Kukumbukira mmene Yehova anatithandizira nthawi ina m’mbuyomu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena