Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 October tsamba 2
  • “Khulupirira Yehova ndi Mtima Wako Wonse”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Khulupirira Yehova ndi Mtima Wako Wonse”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mumakhulupirira Kuti Yehova Amachita Zinthu M’njira Yoyenera?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Muzikhulupirira Yehova Kuti Muzisankha Zochita Mwanzeru
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kodi Mumasankha Bwanji Zochita?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Mmene Mungasankhire Mwanzeru
    Nsanja ya Olonda—2001
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 October tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MIYAMBO 1-6

“Khulupirira Yehova ndi Mtima Wako Wonse”

Munthu akupemphera

Yehova ndi woyenera kuti tizimukhulupirira ndi mtima wonse. Tanthauzo la dzina lake limatithandiza kukhulupirira kuti iye akhoza kukwaniritsa malonjezo ake onse. Kupemphera kungatithandizenso kumukhulupirira. Chaputala 3 cha Miyambo chimatitsimikizira kuti tikamadalira Yehova, ‘adzawongola njira zathu zonse.’

Munthu amene amadalira nzeru zake . . .

3:5-7

  • amasankha zochita popanda kupempha kaye Yehova kuti amuthandize

  • amatsatira maganizo ake kapena a anthu am’dzikoli

Munthu amene amadalira Yehova . . .

  • amaphunzira Baibulo, kuganizira zimene amaphunzirazo ndiponso kupemphera kuti azilimbitsa ubwenzi wake ndi Yehova

  • akamasankha zochita amafufuza mfundo za m’Baibulo kuti adziwe maganizo a Yehova pa nkhaniyo

KODI INEYO NDIMASANKHA BWANJI ZOCHITA?

CHOYAMBA: Ndimasankha zimene ineyo ndikuona kuti ndi zanzeru

CHOYAMBA: Ndimapemphera ndiponso kuphunzira Baibulo kuti ndidziwe maganizo a Yehova pa nkhaniyo

CHACHIWIRI: Ndimapempha Yehova kuti adalitse zimene ndasankhazo

CHACHIWIRI: Ndimasankha zimene zikugwirizana ndi mfundo za m’Baibulo

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena