Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 October tsamba 3
  • “Mtima Wako Usapatuke”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mtima Wako Usapatuke”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Tingateteze Bwanji Mtima Wathu?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Khalani Maso Satana Akufuna Kukumezani
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Khalani ndi Mtima Wovomerezeka kwa Yehova
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
    Galamukani!—2022
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 October tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MIYAMBO 7-11

“Mtima Wako Usapatuke”

Mnyamata akuyang’ana kunyumba kwa mkazi wachiwerewere

Mfundo za Yehova zikhoza kutiteteza. Koma kuti zizitithandiza tiyenera kuzikonda ndi mtima wathu wonse. (Miy. 7:3) Mtumiki wa Yehova akalola kuti mtima wake upatuke, zimakhala zosavuta kuti Satana amupusitse. Chaputala 7 cha Miyambo chimafotokoza za mnyamata wina yemwe analola kuti mtima wake umupusitse. Kodi tingaphunzire chiyani pa zimene zinachitikira mnyamatayu?

  • Diso

    Kuona

    7:10

  • Mkazi wagwira dzanja la mwamuna

    Kukhudza

    7:13

  • Buledi ndi vinyo

    Kulawa

    7:14

  • Mabotolo a perefyumu

    Kumva Fungo

    7:17

  • Mkazi akunong’oneza mwamuna

    Kumva Mawu

    7:21

  • Satana amagwiritsa ntchito zinthu zimene tatchulazi pofuna kusokoneza ubwenzi wathu ndi Yehova

  • Tikakhala anzeru ndiponso omvetsa zinthu tidzatha kuoneratu ndiponso kupewa mavuto amene angabwere ngati titachita zinthu zoipa

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena